Mateyu 12:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngati Ine ndimaturutsa ziwanda ndi mphamvu yace ya Beelzebule, ana anu amaziturutsa ndi mphamvu ya yani? cifukwa cace iwo adzakhala oweruza anu.

Mateyu 12

Mateyu 12:20-29