Mateyu 10:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene angakuzunzeni inu m'mudzi uwu, thawirani mwina: indetu ndinena kwa inu, Simudzaitha mizinda ya Israyeli, kufikira Mwana wa munthu atadza.

Mateyu 10

Mateyu 10:22-25