Mateyu 1:22-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Ndipo zonsezi zinakhala kuti cikacitidwe conenedwa ndi Ambuye mwa mneneri, ndi kuti,

23. Onani namwali adzaima,Nadzabala mwana wamwamuna,Ndipo adzamucha dzina lace, Emanueli;ndilo losandulika, Mulungu nafe.

24. Ndipo Yosefe anauka tulo tace, nacita monga anamuuza mngelo wa Ambuye, nadzitengera yekha mkazi wace;

25. ndipo sanamdziwa iye kufikira atabala rriwana wace; namucha dzina lace Yesu.

Mateyu 1