Masalmo 96:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamaso pa Yehova, pakuti akudza;Pakuti akudza kudzaweruza dziko lapansi:Adzaweruza dziko lokhalamo anthu ndi cilungamo,Ndi mitundu ya anthu ndi coonadi.

Masalmo 96

Masalmo 96:3-13