Masalmo 9:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Adaniwo atha psiti, apululuka nthawi zonse;Ndipo midziyo mwaipasula,Cikumbukilo cao pamodzi catha.

7. Koma Yehova akhala cikhalire:Anakonzeratu mpando wacifumu wace kuti aweruze.

8. Ndipo Iyeyu adzaweruza dziko lapansi m'cilungamo,Nadzaweruza anthu molunjika.

Masalmo 9