Masalmo 79:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Kubuula kwa wandende kufike kuli Inu;Monga mwa mphamvu yanu yaikuru lolani ana a imfa atsale;

12. Ndipo anansi athu amene anatonza Inu muwabwezere cotonza cao,Kasanu ndi kawiri kumtima kwao, Ambuye.

13. Potero ife anthu anu ndi nkhosa za pabusa panuTidzakuyamikani kosatha;Tidzafotokozera cilemekezo canu ku mibadwo mibadwo.

Masalmo 79