58. Ndipo anautsa mtima wace ndi malo amsanje ao,Namcititsa nsanje ndi mafano osema.
59. Pakumva ici Mulungu, anakwiya, Nanyozatu Israyeli;
60. Ndipo anacokera cokhalamo ca ku Silo,Cihemaco adacimanga mwa anthu;
61. Napereka mphamvu yace m'ukapolo,Ndi ulemerero wace m'dzanja la msautsi.