Masalmo 65:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Muceza nalo dziko lapansi, muhthirira,Mulilemeza kwambiri;Mtsinje wa Mulungu udzala nao madzi:Muwameretsera tirigu m'mene munakonzera nthaka.

10. Mukhutitsa nthaka yace yolima;Mufafaniza nthumbira zace?Muiolowetsa ndi mbvumbi;Mudalitsa mmera wace.

11. Mubveka cakaci ndi ukoma wanu;Ndipo mabande anu akukha zakuca.

Masalmo 65