Masalmo 65:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wodala munthuyo mumsankha, ndi kumyandikizitsa,Akhale m'mabwalo anu:Tidzakhuta nazo zokoma za m'nyumba yanu,Za m'malo oyera a Kacisi wanu.

Masalmo 65

Masalmo 65:3-13