Masalmo 64:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Imvani Yehova, mau anga, m'kudandaula kwanga;Sungani moyo wanga angandiopse mdani.

2. Ndibiseni pa upo wacinsinsi wa ocita zoipa;Pa phokoso la ocita zopanda pace:

3. Amene anola lilime lao ngati lupanga,Napiringidza mibvi yao, ndiyo mau akuwawitsa;

4. Kuponyera wangwiro mobisika:Amponyera modzidzimutsa, osaopa.

Masalmo 64