6. Ndalema nako kuusa moyo kwanga;Ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse;Mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga.
7. Lapuwala diso langa cifukwa ca cisoni;Lakalamba cifukwa ca onse akundisautsa.
8. Cokani kwa ine, nonsenu akucita zopanda pace;Pakuti wamva Yehova mau a kulira kwanaa,
9. Wamva Yehova kupemba kwanga;Yehova adzalandira pemphero langa.