Masalmo 55:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Ndipo ndinati, Ha, wina akadandipatsa mapiko onga a njiwaMwenzi nditauluka, ndi kukhaliratu.

7. Onani, ndikadathawira kutari,Ndikadagona m'cipululu.

8. Ndikadafulumira ndipulumukeKu mphepo yolimba ndi namondwe.

9. Aonongeni, Ambuye, gawani lilime lao:Pakuti ndaona ciwawa ndi ndeu m'mudzimo.

Masalmo 55