2. Mulungu awalira m'Ziyoni, mokongola mwangwiro.
3. Adzafika Mulungu wathu, ndipo sadzakhala cete:Moto udzanyeka pankhope pace,Ndipo pozungulira pace padzasokosera kwakukuru.
4. Kumwamba adzaitana zakumwamba,Ndi dziko lapansi, kuti aweruze anthu ace: