Masalmo 31:5-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Ndipereka mzimu wanga m'dzanja lanu:Mwandiombola, Inu Yehova, Mulungu wa coonadi.

6. Ndikwiya nao iwo akusamala zacabe zonama:Koma ndikhulupirira Yehova.

7. Ndidzakondwera ndi kusangalala m'cifundo canu:Pakuti mudapenya zunzo langa;Ndipo mudadziwa mzimu wanga mu nsautso yanga:

Masalmo 31