Masalmo 21:5-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Ulemerero wace ngwaukuru mwa cipulumutso canu:Mumcitira iye ulemu ndi ukulu.

6. Pakuti mumuikira madalitso ku nthawi zonse;Mumkondweretsa ndi cimwemwe pankhope panu.

7. Pakuti mfumu akhulupirira Yehova,Ndipo mwa cifundo ca Wam'mwambamwamba sadzagwedezeka iye,

8. Dzanja lanu lidzapeza adani anu onse:Dzanja lanu lamanja lidzapeza iwo akuda Inu.

Masalmo 21