6. Tsopano ndidziwa kuti Yehova apulumutsa wodzozedwa wace;Adzambvomereza m'Mwamba mwace moyeraNdi mphamvu ya cipulumutso ca dzanja lace lamanja.
7. Ena atama magareca, ndi ena akavalo:Koma ife tidzachula dzina la Yehova Mulungu wathu.
8. Iwowa anagonieka, nagwa:Koma ife tauka, ndipo takhala ciriri.
9. Yehova, pulumutsani,Mfumuyo atibvomereze tsiku lakuitana ife.