Masalmo 20:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Tsopano ndidziwa kuti Yehova apulumutsa wodzozedwa wace;Adzambvomereza m'Mwamba mwace moyeraNdi mphamvu ya cipulumutso ca dzanja lace lamanja.

7. Ena atama magareca, ndi ena akavalo:Koma ife tidzachula dzina la Yehova Mulungu wathu.

8. Iwowa anagonieka, nagwa:Koma ife tauka, ndipo takhala ciriri.

9. Yehova, pulumutsani,Mfumuyo atibvomereze tsiku lakuitana ife.

Masalmo 20