Masalmo 17:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Yehova, imvani cilungamo, mverani mpfuu wanga;Cherani khutu ku pemphero langa losaturuka m'milomo ya cinyengo,

2. Pankhope panu paturuke ciweruzo canga;Maso anu apenyerere zolunjika,

3. Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku;Mwandisuntha, simupeza kanthu;Ndatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa.

4. Za macitidwe a anthu, ndaceniera ndi mau a milomo yanuNdingalowe njira za woononga.

Masalmo 17