Masalmo 147:14-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Ndiyeamene akhalitsamalireanu mumtendere;Akukhutitsani ndi tirigu wakuca bwino.

15. Atumiza lamulo lace ku dziko lapansi;Mau ace athamanga liwiro.

16. Apatsa cipale cofewa ngati ubweya;Awaza cisanu ngati phulusa.

17. Aponya matalala ace ngati zidutsu:Adzaima ndani pa kuzizira kwace?

Masalmo 147