14. Ndiyeamene akhalitsamalireanu mumtendere;Akukhutitsani ndi tirigu wakuca bwino.
15. Atumiza lamulo lace ku dziko lapansi;Mau ace athamanga liwiro.
16. Apatsa cipale cofewa ngati ubweya;Awaza cisanu ngati phulusa.
17. Aponya matalala ace ngati zidutsu:Adzaima ndani pa kuzizira kwace?