Masalmo 135:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Anapanda oyamba a Aigupto,Kuyambira munthu kufikira zoweta.

9. Anatumiza zizindikilo ndi zodabwiza pakati pako,Aigupto iwe, Pa Farao ndi pa omtumikira onse.

10. Ndiye amene anapanda amitundu ambiri.Napha mafumu amphamvu;

Masalmo 135