4. Taonani, wakusunga IsrayeaSadzaodzera kapena kugona.
5. Yehova ndiye wakukusunga;Yehova ndiye mthunzi wako wa ku dzanja lako lamanja.
6. Dzuwa silidzawamba usana,Mwezi sudzakupanda usiku.
7. Yehova adzakusunga kukucotsera zoipa ziri zonse;Adzasunga moyo wako.