Masalmo 121:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndikweza maso anga kumapiri:Thandizo langa lidzera kuti?

2. Thandizo langa lidzera kwa Yehova,Wakulenga zakumwamba ndi dziko lapansi.

3. Sadzalola phazi lako literereke:Iye amene akusunga sadzaodzera.

Masalmo 121