146. Ndinaitanira Inu; ndipulumutseni,Ndipo ndidzasamalira mboni zanu.
147. Ndinapfuula kusanace:Ndinayembekezera mau anu.
148. Maso anga anakumika malonda a usiku,Kuti ndilingirire mau anu.
149. Imvani liu langa monga mwa cifundo canu;Mundipatse moyo monga mwa kuweruza kwanu, Yehova.
150. Otsata zaciwembu andiyandikira;Akhala kutali ndi cilamulo canu.
151. Inu muli pafupi, Yehova;Ndipo malamulo anu onse ndiwo coonadi,