Masalmo 116:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Zingwe za imfa zinandizinga,Ndi zowawa za manda zinandigwira:Ndinapeza nsautso ndi cisoni.

4. Pamenepo ndinaitana dzina la Yehova;Ndikuti, Yehova ndikupemphani landitsani moyo wanga.

5. Yehova ngwa cifundo ndi wolungama;Ndi Mulungu wathu ngwa nsoni.

6. Yehova asunga opusa;Ndidafoka ine, koma anandipulumutsa,

Masalmo 116