9. Israyeli, khulupirira Yehova:Ndiye mthandizi wao ndi cikopa cao.
10. Nyumba ya Aroni, khulupirira Yehova:Ndiye mthandizi wao, ndi cikopa cao.
11. Inu akuopa Yehova, khulupirirani Yehova;Ndiye mthandizi wao ndi cikopa cao.
12. Yehova watikumbukila; adzatidalitsa:Adzadalitsa nyumba ya Israyeli;Adzadalitsa nyumba ya Aroni.
13. Adzadalitsa iwo akuopa Yehova,Ang'ono ndi akuru.