Masalmo 115:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Kwa ife ai, Yehova, kwa ife ai, Koma kwa dzina lanu patsani ulemerero,Cifukwa ca cifundo canu, ndi coonadi canu.

2. Aneneranji amitundu,Ali kuti Mulungu wao?

Masalmo 115