Masalmo 112:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Haleluya.Wodala munthu wakuopa Yehova,Wakukondwera kwambiri ndi malamulo ace,

2. Mbeu yace idzakhala yamphamvu pa dziko lapansi;Mbadwo wa oongoka mtima udzadalitsidwa.

Masalmo 112