3. Anthu anu adzadzipereka eni ace tsiku la camuna canu:M'moyera mokometsetsa, mobadwira tnatanda kuca,Muli nae mame a ubwana wanu.
4. Yehova walamulira, ndipo sadzasintha,Inu ndinu wansembe kosathaMonga mwa cilongosoko ca Melikizedeke.
5. Yehova pa dzanja lamanja lakoAdzaphwanya mafumu tsiku la mkwiyo wace.
6. Adzaweruza mwa amitundu,Adzadzaza dziko ndi mitembo;Adzaphwanya mitu m'maiko ambiri.
7. Adzamwa ku mtsinje wa panjira;Cifukwa cace adzaweramutsa mutu wace.