Masalmo 107:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Ayamike Yehova cifukwa ca cifundo cace,Ndi zodabwiza zace za kwa ana a anthu!

9. Pakuti akhutitsa mtima wolakalaka,Nadzaza mtima wanjala ndi zabwino.

10. Iwo akukhala mumdima ndi mu mthunzi wa imfa,Omangika ndi kuzunzika ndi citsulo;

Masalmo 107