Masalmo 104:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Amene alumikiza mitanda ya zipinda zace m'madzi;Naika makongwa akhale agareta ace;Nayenda pa mapiko a mphepo;

4. Amene ayesa mphepo amithenga ace;Lawi la moto atumiki ace;

5. Anakhazika dziko lapansi pa maziko ace,Silidzagwedezeka ku nthawi yonse.

Masalmo 104