26. ndipo anamva zowawa zambiri ndi asing'anga ambiri, nalipira zonse anali nazo osacira pang'ono ponse, koma makamaka nthenda yace idakula,
27. m'mene iye anamva mbiri yace ya Yesu, anadza m'khamu kumbuyo kwace, nakhudza cobvala cace.
28. Pakuti ananena iye, Ngati ndikakhudza ngakhale zobvala zace ndidzapulumutsidwa.