Marko 13:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pakuti adzauka Akristu onyenga ndi aneneri onyenga, ndipo adzacita zizindikilo ndi zozizwitsa, kuti akasoceretse, ngati nkutheka, osankhidwa omwe.

Marko 13

Marko 13:15-26