13. Anyamata ananyamula mphero,Ana nakhumudwa posenza nkhuni.
14. Akulu adatha kuzipata,Anyamata naleka nyimbo zao.
15. Cimwemwe ca mtima wathu calekeka,Masewera athu asanduka maliro.
16. Korona wagwa pamutu pathu;Kalanga ife! pakuti tinacimwa.
17. Cifukwa ca ici mtima wathu ufoka,Cifukwa ca izi maso athu acita cimbuuzi;
18. Pa phiri la Ziyoni lopasukaloAnkhandwe ayendapo.