Malaki 3:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo iwo akuopa Yehova analankhulana wina ndi mnzace; ndipo Yehova anawachera khutu namva, ndi buku la cikumbutso linalembedwa pamaso pace, la kwa iwo akuopa Yehova, nakumbukila dzina lace.

Malaki 3

Malaki 3:15-18