Malaki 2:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndidana nako kuleka kumene, ati Yehova Mulungu wa Israyeli, ndi iye wakukuta cobvala cace ndi ciwawa, ati Yehova wa makamu; cifukwa cace sungani mzimu wanu kuti musacite mosakhulupirika.

Malaki 2

Malaki 2:13-17