Malaki 2:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo tsono, ansembe inu, lamulo ili ndi la kwa inu.

2. Mukapanda kumvera, mukapanda kuliika mumtima mwanu, kupatsa dzina langa ulemerero, ati Yehova wa makamu, ndidzakutumizirani temberero, ndi kutemberera madalitso anu; inde, ndawatemberera kale cifukwa simuliika mumtima.

Malaki 2