Macitidwe 28:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mtima wa anthu awa watupatu,Ndipo m'makutu mwao mmolemakumva,Ndipo masoao anawatseka;Kuti angaone ndi maso,Nangamve ndi makutu,Nangazindikire ndi mtima,Nangatembenuke,Ndipo Ine ndingawaciritse.

Macitidwe 28

Macitidwe 28:21-31