Macitidwe 26:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinawalanga kawiri kawiri m'masunagoge onse, ndi kuwakakamiza anene zamwano; ndipo pakupsa mtima kwakukuru pa iwo ndinawalondalonda ndi kuwatsata ngakhale kufikira ku midzi yakunja.

Macitidwe 26

Macitidwe 26:10-21