Macitidwe 21:4-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Ndipo m'mene tinapeza ophunzira, tinakhalako masikuasanu ndi awiri; ndipo iwowa ananena ndi Paulo mwa Mzimu, kuti asakwere ku Yerusalemu.

5. Ndipo kunali pamene tidatsiriza masikuwa, tidacoka ndi kunka ulendo wathu; ndipo iwo onse, akazi ndi ana anatiperekeza kufikira kuturuka m'mudzi; ndipo pogwadira pa mcenga wa kunyanja, tinapemphera,

6. ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao.

Macitidwe 21