Macitidwe 20:37-38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

37. Ndipo onsewa analira kwambiri, namkupatira Paulo pakhosi pace, nampsompsona,

38. nalira makamaka cifukwa ca mau adanenawa, kuti sadzaonanso nkhope yace. Ndipo anamperekeza iye kungalawa.

Macitidwe 20