Macitidwe 19:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene mlembi adatontholetsa khamulo, anati, Amuna a Efeso inu, munthuyu ndani wosadziwa kuti mudzi wa Aefeso ndiwo wosungira kacisi wa Artemi wamkuru, ndi fano Iidacokera kwa Zeu?

Macitidwe 19

Macitidwe 19:26-41