Macitidwe 16:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anatimva mkazi wina dzina lace Lidiya, wakugulitsa cibakuwa, wa ku mudzi wa Tiyatira, amene anapembedza Mulungu; mtima wace Ambuye anatsegula, kuti amvere zimene anazinena Paulo.

Macitidwe 16

Macitidwe 16:10-21