Macitidwe 15:33-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Pamene anakhala nthawi, abale analawirana nao ndi mtendere amuke kwa iwo amene anawatumiza. [

34. ]

35. Koma Paulo ndi Bamaba anakhalabe m'Antiokeya, nalinkuphunzitsa, ndi kulalikira mau a Ambuye pamodzi ndi ena ambiri.

36. Patapita masiku, Paulo anati kwa Bamaba, Tibwerenso, tizonde abale m'midzi yonse m'mene tinalalikiramo mau a Ambuye, tione mkhalidwe wao.

37. Ndipo Bamaba anafuna kumtenga Yohane uja, wochedwa Marko.

Macitidwe 15