Macitidwe 14:24-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. Ndipo anapitirira pa Pisidiya, nafika ku Pamfuliya.

25. Ndipo atalankhula mau m'Perge, anatsikira ku Ataliya;

26. komweko anacoka m'ngalawa kunka ku Antiokeya, kumene anaikizidwa ku cisomo ca Mulungu ku Ilchito imene adaimarizayo,

Macitidwe 14