Luka 7:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace, ndinena kwa iwe, Macimo ace, ndiwo ambiri, akhululukidwa; cifukwa anakonda kwambiri; koma munthu amene anamkhululukira pang'ono, iye akonda pang'ono.

Luka 7

Luka 7:46-50