Luka 7:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mwana wa munthu wafika wakudya ndi wakumwa; ndipo munena, Onani, munthu wosusuka ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi anthu ocimwa!

Luka 7

Luka 7:26-38