Luka 7:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atacoka amithenga ace a Yohane, iye anayamba kunena za Yohane kwa anthu a makamu aja, nati, Munaturuka kunka kucipululu kukapenya ciani? Bango logwedezeka ndi mphepo kodi?

Luka 7

Luka 7:23-33