Luka 5:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo cimodzimodzinso Yakobo ndi Yohane, ana a Zebedayo, amene anali anzace a Simoni. Ndipo Yesu anati kwa Simoni, Usaope, kuyambira tsopano udzakhala msodzi wa anthu.

Luka 5

Luka 5:3-15