Luka 23:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo khamu lonselo Iinanyamuka kupita naye kwa Pilato.

2. Ndipo anayamba kumnenera iye, kuti, Tinapeza munthu uyu alikupandutsa anthu a mtundu wathu, ndi kuwaletsa kupereka msonkho kwa Kaisara, nadzinenera kuti iye yekha ndiye Kristu mfumu.

3. Ndipo Pilato anamfunsa iye, nanena, Kodindiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo iye anamyankha nati, Mwatero.

Luka 23