Luka 22:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene iye anali cilankhulire, taonani, khamu la anthu, ndipo iye wochedwa Yudase, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anawatsogolera; nayandikira Yesu kumpsompsona iye.

Luka 22

Luka 22:43-55