Luka 22:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma sipadzatero ndi inu; komatu iye ali wamkuru mwa inu, akhale ngati wamng'ono; ndi iye ali woyamba, akhale ngati wotumikira.

Luka 22

Luka 22:20-31